Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 138:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ngakhale kuti Yehova ali pamwamba, amaona wodzichepetsa,+

      Koma wodzikuza samuyandikira.+

  • Miyambo 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chifukwa cha kudzikuza, munthu amangoyambitsa mavuto,+ koma anthu amene amakhala pamodzi n’kumakambirana amakhala ndi nzeru.+

  • Agalatiya 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti ngati wina akudziona kuti ndi wofunika pamene si wotero,+ akudzinyenga.

  • Yakobo 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Abale, pa nkhani ya kumva zowawa+ ndi kuleza mtima,+ tengerani chitsanzo+ kwa aneneri+ amene analankhula m’dzina la Yehova.+

  • 1 Petulo 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chimodzimodzinso inu anyamata. Muzigonjera+ amuna achikulire. Koma nonsenu muzichitirana zinthu modzichepetsa,+ chifukwa Mulungu amatsutsa odzikweza, koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena