Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndi amene akuyenda mosalakwitsa zinthu,+ amene amachita chilungamo,+

      Ndi kulankhula zoona mumtima mwake.+

  • Salimo 77:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Usiku ndidzakumbukira nyimbo zanga zoimbidwa ndi chipangizo cha zingwe.+

      Ndidzasonyeza kudera nkhawa mumtima mwanga,+

      Ndipo ndidzasinkhasinkha zinthu zonse mozama.

  • Miyambo 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nzeru zikalowa mumtima mwako,+ ndipo kudziwa zinthu kukakhala kosangalatsa m’moyo wako,+

  • Miyambo 15:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mtima wa munthu wolungama umayamba waganiza usanayankhe,+ koma pakamwa pa anthu oipa pamasefukira zoipa.+

  • Mateyu 12:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Munthu wabwino amatulutsa zabwino m’chuma chake chabwino,+ koma munthu woipa amatulutsa zoipa m’chuma chake choipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena