Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ubwenzi wolimba ndi Yehova ndi wa anthu amene amamuopa,+

      Pangano lakenso ndi la anthu oterowo, ndipo iye amawadziwitsa panganolo.+

  • Salimo 34:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Opani Yehova, inu oyera ake,+

      Pakuti onse omuopa sasowa kanthu.+

  • Salimo 103:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Monga mmene bambo amasonyezera chifundo kwa ana ake,+

      Yehova wasonyezanso chifundo kwa onse omuopa.+

  • Miyambo 23:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mtima wako usamasirire anthu ochimwa,+ koma iwe uziopa Yehova tsiku lonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena