Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 46:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Mulungu ndiye pothawira pathu ndi mphamvu yathu,+

      Thandizo lopezeka mosavuta pa nthawi ya masautso.+

  • Salimo 121:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Yehova adzakuteteza ku masoka onse.+

      Iye adzateteza moyo wako.+

  • Nahumu 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova ndi wabwino+ ndipo ndi malo achitetezo+ pa tsiku la nsautso.+

      Amadziwa amene amathawira kwa iye kuti apeze chitetezo.+

  • Zefaniya 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mwa iwe ndidzasiyamo anthu ena, odzichepetsa ndi ofatsa,+ ndipo amenewa adzapeza chitetezo m’dzina la Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena