Yeremiya 23:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Mobwerezabwereza iwo akuuza anthu amene sakundilemekeza kuti, ‘Yehova wanena kuti: “Anthu inu mudzakhala pa mtendere.”’+ Ndipo aliyense woumitsa mtima wake+ akumuuza kuti, ‘Tsoka silidzakugwerani anthu inu.’+ Ezekieli 13:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Amuna inu, kodi masomphenya mwaonawa si abodza? Kodi zimene mwaloserazi si zonama? Inu mwati, ‘Yehova wanena kuti,’ pamene ine sindinalankhule kalikonse.”’+ Mika 2:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Munthu wolondola zinthu zopanda pake ndi zachinyengo akanena bodza lakuti:+ “Ndidzakulosererani zokhudza vinyo ndi chakumwa choledzeretsa,” ndiye adzakhale mneneri wa anthu awa.+ 2 Timoteyo 4:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pakuti idzafika nthawi imene anthu sadzafunanso chiphunzitso cholondola,+ koma mogwirizana ndi zilakolako zawo, adzadzipezera aphunzitsi kuti amve zowakomera m’khutu.+
17 Mobwerezabwereza iwo akuuza anthu amene sakundilemekeza kuti, ‘Yehova wanena kuti: “Anthu inu mudzakhala pa mtendere.”’+ Ndipo aliyense woumitsa mtima wake+ akumuuza kuti, ‘Tsoka silidzakugwerani anthu inu.’+
7 Amuna inu, kodi masomphenya mwaonawa si abodza? Kodi zimene mwaloserazi si zonama? Inu mwati, ‘Yehova wanena kuti,’ pamene ine sindinalankhule kalikonse.”’+
11 Munthu wolondola zinthu zopanda pake ndi zachinyengo akanena bodza lakuti:+ “Ndidzakulosererani zokhudza vinyo ndi chakumwa choledzeretsa,” ndiye adzakhale mneneri wa anthu awa.+
3 Pakuti idzafika nthawi imene anthu sadzafunanso chiphunzitso cholondola,+ koma mogwirizana ndi zilakolako zawo, adzadzipezera aphunzitsi kuti amve zowakomera m’khutu.+