Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 115:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mafano awo ndi opangidwa ndi siliva ndi golide,+

      Ntchito ya manja a munthu wochokera kufumbi.+

  • Salimo 135:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mafano a anthu a mitundu ina ndi opangidwa ndi siliva ndi golide,+

      Ntchito ya manja a munthu wochokera kufumbi.+

  • Yesaya 37:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Atentha milungu yawo pamoto,+ chifukwa sinali milungu,+ koma ntchito ya manja a anthu,+ mitengo ndi miyala, n’chifukwa chake anaiwononga.+

  • Yesaya 41:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Chotero mmisiri wa mitengo anali kulimbikitsa mmisiri wa zitsulo.+ Amene anali kusalaza zitsulo ndi nyundo anali kulimbikitsa amene anali kumenya zitsulo ndi nyundo. Ponena za ntchito yowotcherera zitsulo ndi mtovu, iye anati: “Zili bwino.” Pomalizira pake, wina anakhomerera fanolo ndi misomali kuti lisagwedezeke.+

  • Hoseya 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Zimenezi zachokera ku Isiraeli.+ Mmisiri ndiye anapanga fano la mwana wa ng’ombe la ku Samariya.+ Fanolo si Mulungu woona, chifukwa lidzangokhala ngati nkhuni zowazawaza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena