Yesaya 44:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Munthu wogoba zitsulo ndi chogobera watentha chitsulocho ndi makala amoto. Wachiwongola ndi nyundo, ndipo wakhala ali jijirijijiri kuchiumba ndi dzanja lake lamphamvu.+ Wamva njala ndipo alibe mphamvu. Sanamwe madzi, chotero watopa. Yesaya 46:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pali anthu amene amakhuthula golide m’zikwama, ndi kuyeza siliva pasikelo. Iwo amalemba ganyu mmisiri wa zitsulo ndipo iye amapanga mulungu ndi zinthu zimenezi.+ Kenako anthuwo amayamba kuweramira ndi kugwadira mulunguyo.+
12 Munthu wogoba zitsulo ndi chogobera watentha chitsulocho ndi makala amoto. Wachiwongola ndi nyundo, ndipo wakhala ali jijirijijiri kuchiumba ndi dzanja lake lamphamvu.+ Wamva njala ndipo alibe mphamvu. Sanamwe madzi, chotero watopa.
6 Pali anthu amene amakhuthula golide m’zikwama, ndi kuyeza siliva pasikelo. Iwo amalemba ganyu mmisiri wa zitsulo ndipo iye amapanga mulungu ndi zinthu zimenezi.+ Kenako anthuwo amayamba kuweramira ndi kugwadira mulunguyo.+