Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Komano ngati mukufuna kuwakhululukira tchimo lawo,+ . . . koma ngati simukufuna, ndifafanizeni+ chonde, m’buku lanu+ limene mwalemba.”

  • Chivumbulutso 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho amene wapambana pa nkhondo+ adzavekedwa malaya akunja oyera.+ Ndipo sindidzafafaniza dzina lake m’buku la moyo,+ koma ndidzavomereza dzina lake pamaso pa Atate wanga,+ ndi pamaso pa angelo ake.+

  • Chivumbulutso 20:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Komanso, aliyense amene sanapezeke atalembedwa m’buku la moyo+ anaponyedwa m’nyanja yamoto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena