Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 69:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Afafanizidwe m’buku la anthu amoyo,+

      Ndipo iwo asalembedwe m’bukumo pamodzi ndi anthu olungama.+

  • Danieli 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Pa nthawi imeneyo Mikayeli,+ kalonga wamkulu+ amene waimirira+ kuti athandize anthu a mtundu wako, adzaimirira.+ Ndiyeno padzafika nthawi ya masautso imene sinakhalepo kuyambira pamene mtundu woyambirira wa anthu unakhalapo kufikira nthawi imeneyo.+ Pa nthawi imeneyo aliyense mwa anthu a mtundu wako amene dzina lake lidzakhala litalembedwa m’buku+ adzapulumuka.+

  • Afilipi 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndikupempha iwenso wantchito mnzanga weniweni,+ kuti upitirize kuwathandiza amayi amenewa. Iwo ayesetsa limodzi ndi ine pa ntchito+ ya uthenga wabwino. Achita zimenezi limodzinso ndi Kilementi ndi antchito anzanga ena onse,+ amene mayina awo+ ali m’buku la moyo.+

  • Chivumbulutso 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho amene wapambana pa nkhondo+ adzavekedwa malaya akunja oyera.+ Ndipo sindidzafafaniza dzina lake m’buku la moyo,+ koma ndidzavomereza dzina lake pamaso pa Atate wanga,+ ndi pamaso pa angelo ake.+

  • Chivumbulutso 17:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chilombo chimene waona, chinalipo,+ tsopano palibe, komabe chili pafupi kutuluka kuphompho,+ ndipo chidzapita ku chiwonongeko. Anthu okhala padziko lapansi akaona kuti chilombocho chinalipo, tsopano palibe, komabe chidzakhalapo, adzadabwa kwambiri pochita nacho chidwi. Koma mayina awo sanalembedwe mumpukutu wa moyo+ kuyambira pa kukhazikitsidwa kwa dziko.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena