Deuteronomo 28:48 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 48 Udzatumikira adani ako+ amene Yehova adzawatuma kuti akuukire. Udzawatumikira uli ndi njala,+ ludzu, usiwa ndiponso ukusowa china chilichonse. Adzakuveka goli lachitsulo m’khosi lako kufikira atakufafaniza.+ Salimo 22:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Mphamvu yanga yauma gwaa, ngati phale.+Lilime langa lamamatira kunkhama zanga,+Ndipo mwandikhazika m’fumbi la imfa.+ Maliro 4:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Lilime la ana oyamwa lamamatira kummero chifukwa cha ludzu.+Ana apempha chakudya+ koma palibe amene akuwapatsa.+ Luka 16:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Choncho anaitana kuti, ‘Atate Abulahamu,+ ndichitireni chifundo. Mutume Lazaro kuti aviike nsonga ya chala chake m’madzi kuti aziziritse lilime langa,+ chifukwa ndikuzunzika m’moto wolilimawu.’+
48 Udzatumikira adani ako+ amene Yehova adzawatuma kuti akuukire. Udzawatumikira uli ndi njala,+ ludzu, usiwa ndiponso ukusowa china chilichonse. Adzakuveka goli lachitsulo m’khosi lako kufikira atakufafaniza.+
15 Mphamvu yanga yauma gwaa, ngati phale.+Lilime langa lamamatira kunkhama zanga,+Ndipo mwandikhazika m’fumbi la imfa.+
4 Lilime la ana oyamwa lamamatira kummero chifukwa cha ludzu.+Ana apempha chakudya+ koma palibe amene akuwapatsa.+
24 Choncho anaitana kuti, ‘Atate Abulahamu,+ ndichitireni chifundo. Mutume Lazaro kuti aviike nsonga ya chala chake m’madzi kuti aziziritse lilime langa,+ chifukwa ndikuzunzika m’moto wolilimawu.’+