Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 13:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Ndidzachititsa Amedi kuti awaukire.+ Iwowa amaona kuti siliva si kanthu, ndipo sasangalala ndi golide.

  • Yesaya 41:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 “Ine ndautsa winawake kuchokera kumpoto, ndipo abwera.+ Iye adzaitana pa dzina langa kuchokera kotulukira dzuwa.+ Adzaukira atsogoleri ngati kuti ndi dongo+ ndiponso ngati kuti iyeyo ndi woumba amene amapondaponda dongo laliwisi.

  • Yeremiya 51:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Iwe ndiwe chibonga changa, zida zanga zankhondo.+ Kudzera mwa iwe ndidzaphwanya mitundu ya anthu kukhala zidutswazidutswa. Kudzera mwa iwe ndidzawononga maufumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena