Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 137:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iwe mwana wamkazi wa Babulo, amene udzafunkhidwa,+

      Wodala ndi amene adzakubwezera+

      Zimene iwe watichitira.+

  • Yeremiya 50:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Iwo amadziwa kuponya mivi ndi uta komanso nthungo.+ Amenewo ndi anthu ankhanza ndipo sadzakumvera chifundo.+ Phokoso lawo lili ngati phokoso la nyanja yowinduka.+ Adzakwera pamahatchi+ ndi kukuzungulira mogwirizana n’cholinga choti akuthire nkhondo, iwe mwana wamkazi wa Babulo.+

  • Zekariya 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Fulumira Ziyoni!+ Thawa, iwe amene ukukhala ndi mwana wamkazi wa Babulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena