Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 17:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Aliyense wonena kuti munthu woipa ndi wolungama+ ndiponso aliyense wonena kuti munthu wolungama ndi woipa,+ onsewa ndi onyansa kwa Yehova.+

  • Malaki 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Anthu inu mwatopetsa Yehova ndi mawu anu,+ ndipo mwanena kuti, ‘Tamutopetsa motani?’ Mwa kunena kuti, ‘Aliyense wochita zoipa ndi wabwino kwa Yehova, ndipo iye amakondwera ndi anthu otero.’+ Kapena mwa kunena kuti, ‘Kodi Mulungu wachilungamo ali kuti?’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena