Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 16:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndipo Aroni aziika manja ake onse+ pamutu pa mbuziyo ndi kuvomereza+ zolakwa zonse+ za ana a Isiraeli ndiponso kusamvera kwawo m’machimo awo onse.+ Zonsezi aziziika pamutu pa mbuzi ija+ ndi kuipereka kwa munthu amene am’sankhiratu+ kuti akaisiye kuchipululu.+

  • Mateyu 26:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Popita kumeneko anatenga Petulo ndi ana awiri+ a Zebedayo. Ndipo anayamba kumva chisoni ndi kuvutika kwambiri mumtima mwake.+

  • Luka 19:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Tsopano atayandikira mzinda wa Yerusalemu, anaona mzindawo n’kuyamba kuulirira.+

  • Yohane 11:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yesu anagwetsa misozi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena