Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:136
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 136 Misozi yatsika m’maso mwanga ngati mitsinje ya madzi,+

      Chifukwa chakuti iwo sanasunge chilamulo chanu.+

  • Yeremiya 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndikanakonda kuti m’mutu mwanga mukhale madzi ambiri ndiponso kuti maso anga akhale magwero a misozi.+ Pamenepo ndikanalira usana ndi usiku chifukwa cha anthu ophedwa a mwana wamkazi wa anthu anga.+

  • Luka 23:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Yesu anacheukira amayiwo ndi kunena kuti: “Ana aakazi a Yerusalemu inu, lekani kundilirira. Koma mudzilirire nokha ndi ana anu.+

  • Yohane 11:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yesu anagwetsa misozi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena