Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kuti apulumutse moyo wawo ku imfa,+

      Ndi kuwasunga ndi moyo pa nthawi ya njala.+

  • Salimo 37:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pa nthawi yatsoka sadzachita manyazi,+

      Ndipo pa nthawi ya njala adzakhuta.+

  • Yesaya 33:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iye ndi amene adzakhale pamalo apamwamba.+ Malo ake okhala adzakhala otetezeka m’matanthwe movuta kufikamo.+ Iye adzapatsidwa chakudya+ ndipo madzi ake sadzatha.”+

  • Hoseya 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ine ndinakudziwa uli m’chipululu,+ m’dziko la matenda otenthetsa thupi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena