Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 49:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iweyo udzanenadi mumtima mwako kuti, ‘Kodi bambo wa ana amene ndaberekawa ndani, popeza ine ndine mayi woferedwa ana ndiponso wosabereka, mayi yemwe anatengedwa kupita kudziko lina ku ukaidi?+ Nanga ana awa, anawalera ndani?+ Inetu ndinasiyidwa m’mbuyo ndekhandekha.+ Ndiyeno ana awa anali kuti?’”+

  • Hagai 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “‘Ndigwedeza mitundu yonse ya anthu, ndipo zinthu zamtengo wapatali zochokera ku mitundu yonse ya anthu zidzalowa m’nyumba imeneyi.+ Ine ndidzadzaza nyumbayi ndi ulemerero,’+ watero Yehova wa makamu.

  • Yohane 10:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Ndili ndi nkhosa zina+ zimene sizili za khola ili,+ zimenezonso ndiyenera kuzibweretsa. Zidzamva mawu anga,+ ndipo zidzakhala gulu limodzi ndi m’busa mmodzi.+

  • Chivumbulutso 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno mmodzi wa akulu+ aja anandifunsa kuti: “Kodi amene avala mikanjo yoyerawa+ ndi ndani, ndipo achokera kuti?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena