Salimo 102:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Inu mudzanyamuka ndi kusonyeza Ziyoni chifundo,+Pakuti imeneyi ndi nyengo yomukomera mtima,Chifukwa nthawi yoikidwiratu yakwana.+ Yesaya 43:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 “Komanso, nthawi zonse ine sindisintha.+ Palibenso wina amene angathe kupulumutsa anthu m’dzanja langa.+ Ndikayamba kuchitapo kanthu,+ ndani amene angalimbane ndi dzanja langa?”+
13 Inu mudzanyamuka ndi kusonyeza Ziyoni chifundo,+Pakuti imeneyi ndi nyengo yomukomera mtima,Chifukwa nthawi yoikidwiratu yakwana.+
13 “Komanso, nthawi zonse ine sindisintha.+ Palibenso wina amene angathe kupulumutsa anthu m’dzanja langa.+ Ndikayamba kuchitapo kanthu,+ ndani amene angalimbane ndi dzanja langa?”+