Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 19:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Awa ndi mawu otsutsana naye amene Yehova wanena:

      “Namwali, mwana wamkazi wa Ziyoni, wakunyoza+ ndipo wakuseka.+

      Kumbuyo kwako, mwana wamkazi wa Yerusalemu+ wakupukusira mutu.+

  • Salimo 132:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yehova wasankha Ziyoni,+

      Ndipo amafunitsitsa kuti akhale malo ake okhalamo. Iye amati:+

  • Yesaya 10:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Chotero Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa,+ wanena kuti: “Anthu anga amene mukukhala m’Ziyoni,+ musachite mantha chifukwa cha Msuri amene anali kukukwapulani ndi chikwapu+ ndiponso kukumenyani ndi ndodo, ngati mmene Iguputo anali kuchitira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena