Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anthu inu, imbani nyimbo motsagana ndi zipangizo zoimbira, kutamanda Yehova amene akukhala m’Ziyoni.+

      Fotokozani ntchito zake kwa mitundu ya anthu.+

  • Salimo 48:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Munsanja zokhalamo za m’mudzimo, Mulungu wadziwika kuti ndi malo okwezeka ndiponso achitetezo.+

  • Salimo 74:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Kumbukirani anthu amene munawatenga kukhala anu kalelo,+

      Fuko limene munaliwombola monga cholowa chanu,+

      Ndi phiri la Ziyoni ili mmene inu mukukhala.+

  • Salimo 76:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Malo ake opumulirako ali ku Salemu,+

      Malo ake okhalamo ali ku Ziyoni.+

  • Salimo 78:68
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 68 Koma anasankha fuko la Yuda,+

      Phiri la Ziyoni limene analikonda.+

  • Salimo 135:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Yehova amene akukhala ku Yerusalemu,+

      Atamandidwe mu Ziyoni.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Aheberi 12:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma m’malomwake, inu mwafika kuphiri la Ziyoni+ ndi mzinda+ wa Mulungu wamoyo, Yerusalemu wakumwamba,+ kumene kuli angelo miyandamiyanda,*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena