Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 66:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Bwerani anthu inu, kuti muone ntchito za Mulungu.+

      Zimene wachitira ana a anthu ndi zochititsa mantha.+

  • Salimo 96:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nenani pakati pa anthu a mitundu ina kuti: “Yehova wakhala mfumu.+

      Dziko lapansi nalonso lakhazikika moti silingagwedezeke.+

      Iye adzaweruzira mitundu ya anthu milandu yawo mwachilungamo.”+

  • Salimo 105:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 105 YAMIKANI Yehova, itanani pa dzina lake,+

      Lengezani zochita zake pakati pa mitundu ya anthu.+

  • Salimo 107:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iwo apereke nsembe zoyamikira,+

      Ndi kulengeza za ntchito zake ndi mfuu yachisangalalo.+

  • Yesaya 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 M’tsiku limenelo mudzanenadi kuti: “Yamikani Yehova anthu inu.+ Itanani pa dzina lake.+ Dziwitsani mitundu ya anthu zochita zake.+ Nenani kuti dzina lake n’lokwezeka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena