Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anthu inu, imbani nyimbo motsagana ndi zipangizo zoimbira, kutamanda Yehova amene akukhala m’Ziyoni.+

      Fotokozani ntchito zake kwa mitundu ya anthu.+

  • Salimo 40:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inu Yehova Mulungu wanga, mwatichitira zinthu zambiri zodabwitsa,+

      Ndipo mumatiganizira.+

      Palibe angafanane ndi inu.+

      Ndikafuna kulankhula ndi kunena za zodabwitsazo,

      Zimachuluka kwambiri moti sindingathe kuzifotokoza.+

  • Salimo 105:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Muimbireni, muimbireni nyimbo zomutamanda,+

      Sinkhasinkhani ntchito zake zonse zodabwitsa.+

  • Salimo 145:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Anthu adzatamanda ntchito zanu ku mibadwomibadwo,+

      Ndipo adzasimba za zochita zanu zamphamvu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena