Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 25:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti dzanja la Yehova lidzakhazikika paphiri limeneli,+ ndipo Mowabu adzapondedwapondedwa+ pamalo pake ngati mulu wa udzu umene umapondedwapondedwa pamalo opangira manyowa.+

  • Amosi 9:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndidzachita zimenezi kuti anthu anga adzatenge zinthu zotsala za Edomu+ ndi mitundu yonse ya anthu imene inali kuitanira pa dzina langa,’+ watero Yehova, amene akuchita zimenezi.

  • Obadiya 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Nyumba ya Yakobo idzakhala ngati moto,+ nyumba ya Yosefe idzakhala ngati malawi a moto ndipo nyumba ya Esau idzakhala ngati mapesi.+ Motowo udzayatsa mapesiwo ndi kuwanyeketsa. Sipadzakhala wopulumuka aliyense wa nyumba ya Esau,+ pakuti Yehova mwiniyo wanena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena