Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti nyumba yake imatsikira kumanda ndipo njira zake zimatsikira kwa akufa.+

  • Mlaliki 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zonse zimapita kumalo amodzi.+ Zonse zinachokera kufumbi+ ndipo zonse zimabwerera kufumbi.+

  • Yesaya 26:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iwo afa. Sadzakhalanso ndi moyo.+ Iwo ndi akufa+ ndipo sadzaukanso.+ Pa chifukwa chimenechi, mwawatembenukira kuti muwawononge n’cholinga choti asadzatchulidwenso.+

  • Ezekieli 32:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “‘Ku Mandako, atsogoleri a anthu amphamvu adzalankhula ndi iyeyo komanso amene anali kumuthandiza.+ Onsewo adzatsikira kumanda.+ Iwo adzaphedwa ndi lupanga ndipo adzaikidwa m’manda mofanana ndi anthu osadulidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena