Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 1:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 komanso m’chipululu,+ kumene munaona mmene Yehova Mulungu wanu anakunyamulirani.+ M’njira yonse imene munayenda anakunyamulani ngati mmene bambo amanyamulira mwana wake, mpaka kufika malo ano.’+

  • Ezekieli 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Unali kuvala zinthu zagolide ndi zasiliva ndiponso nsalu zabwino kwambiri. Unali kuvala nsalu zamtengo wapatali ndi chovala cha nsalu yopeta.+ Unkadya ufa wosalala, uchi, ndi mafuta+ ndipo unakhala chiphadzuwa. Patapita nthawi unakhala woyenera ufumu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena