-
Deuteronomo 32:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Anapitiriza kumuyendetsa pamapiri a dziko lapansi,+
Moti anadya zokolola za m’minda.+
Anapitirizanso kumudyetsa uchi wochokera m’thanthwe,+
Ndi mafuta ochokera m’mwala wa nsangalabwi.+
-