Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Okhulupirika, iye amawakhalitsa chete,

      Ndipo amuna okalamba, iye amawachotsera nzeru.

  • Yobu 12:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Amachotsa nzeru za atsogoleri a anthuwo,

      Kuti iwo aziyendayenda kumalo kopanda kanthu,+ kumene kulibe njira.

  • Yesaya 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Anthu a mu Iguputo adzadabwa kwambiri+ ndipo ine ndidzasokoneza zolinga za dzikolo.+ Iwo adzafunsira kwa milungu yopanda pake,+ kwa anthu amatsenga, kwa olankhula ndi mizimu ndiponso kwa olosera zam’tsogolo.+

  • 2 Atesalonika 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ichi n’chifukwa chake Mulungu walola kuti iwo anyengedwe ndipo azikhulupirira bodza,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena