Yesaya 1:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 1 Masomphenya+ amene Yesaya+ mwana wa Amozi anaona, okhudza Yuda ndi Yerusalemu m’masiku a Uziya,+ Yotamu,+ Ahazi+ ndi Hezekiya,+ mafumu a Yuda:+ Yesaya 13:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Uwu ndi uthenga wokhudza Babulo,+ umene Yesaya mwana wa Amozi+ anaona m’masomphenya: Yesaya 22:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Pakuti Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa, wabweretsa tsiku lachisokonezo,+ la kugonjetsedwa+ ndiponso lothetsa nzeru+ m’chigwa cha masomphenya. Kumeneko mpanda ukugwetsedwa+ ndipo kufuula kukumvekera m’phiri.+ Yeremiya 6:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pakuti Yehova wa makamu wanena kuti: “Dulani mitengo+ kuti tipangire Yerusalemu chiunda chomenyerapo nkhondo.*+ Yerusalemu ndi mzinda woyenera kuimbidwa mlandu.+ Mkati mwake muli kuponderezana kokhakokha.+
1 Masomphenya+ amene Yesaya+ mwana wa Amozi anaona, okhudza Yuda ndi Yerusalemu m’masiku a Uziya,+ Yotamu,+ Ahazi+ ndi Hezekiya,+ mafumu a Yuda:+
5 Pakuti Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa, wabweretsa tsiku lachisokonezo,+ la kugonjetsedwa+ ndiponso lothetsa nzeru+ m’chigwa cha masomphenya. Kumeneko mpanda ukugwetsedwa+ ndipo kufuula kukumvekera m’phiri.+
6 Pakuti Yehova wa makamu wanena kuti: “Dulani mitengo+ kuti tipangire Yerusalemu chiunda chomenyerapo nkhondo.*+ Yerusalemu ndi mzinda woyenera kuimbidwa mlandu.+ Mkati mwake muli kuponderezana kokhakokha.+