Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 27:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Zinthu zimene unasunga+ zikafika kumtunda+ zinali kukwanira mitundu yambiri ya anthu.+ Mafumu a padziko lapansi analemera chifukwa cha zinthu zako zochuluka zamtengo wapatali ndi katundu wako wogulitsa.+

  • Ezekieli 28:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Chifukwa chakuti ndiwe wanzeru ndiponso wozindikira, wapanga chuma ndipo ukupitiriza kusonkhanitsa golide ndi siliva m’nyumba zako zosungiramo zinthu.+

  • Yoweli 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chifukwa chakuti anthu inu mwatenga siliva ndi golide wanga,+ mwabweretsa zinthu zanga zamtengo wapatali mu akachisi anu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena