18 Mitunduyo ndi iyi: Yerusalemu ndi mizinda ya Yuda pamodzi ndi mafumu ake ndi akalonga ake. Ndinawamwetsa kuti mizinda yawo ikhale bwinja, chinthu chodabwitsa+ chimene anthu azidzachiimbira mluzu, ndiponso kuti ikhale yotembereredwa. Zimenezi zatsala pang’ono kuchitika.+