Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamenepo Yeremiya anauza Zedekiya kuti: “Yehova Mulungu wa makamu,+ Mulungu wa Isiraeli,+ wanena kuti, ‘Mukadzipereka kwa akalonga a mfumu ya Babulo,+ mudzakhalabe ndi moyo ndipo mzinda uwu sadzautentha, komanso inuyo ndi banja lanu mudzakhalabe ndi moyo.+

  • Yeremiya 39:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “‘Pakuti ine ndidzakupulumutsa ndithu, ndipo sudzaphedwa ndi lupanga, koma udzapulumutsa moyo wako+ chifukwa chakuti wandikhulupirira,’+ watero Yehova.”

  • Yeremiya 45:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma iwe, ukufunafunabe zinthu zazikulu.+ Leka kuzifunafuna.”’+

      “‘Anthu onse ndikuwagwetsera tsoka+ ndipo iwe ndidzakupatsa moyo wako monga chofunkha chako kulikonse kumene ungapite,’ watero Yehova.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena