Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pa nkhondoyo iwo anathandizidwa moti Ahagara ndi onse amene anali nawo anaperekedwa m’manja mwawo, popeza anapempha Mulungu kuti awathandize+ ndipo iye anamva kupembedzera kwawo chifukwa anam’khulupirira.+

  • Salimo 37:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Khulupirira Yehova ndipo chita zabwino.+

      Khala padziko lapansi, ndipo khala wokhulupirika m’zochita zako zonse.+

  • Salimo 37:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Yehova adzawathandiza ndi kuwapulumutsa.+

      Adzawapulumutsa kwa anthu oipa ndi kuwalanditsa,+

      Chifukwa athawira kwa iye.+

  • Salimo 84:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Yehova wa makamu, wodala ndi munthu amene amakhulupirira inu.+

  • Yeremiya 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Wodala ndi munthu aliyense amene amakhulupirira Yehova, amene amadalira Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena