-
Yeremiya 21:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 “‘Yehova wanena kuti: “Kenako Zedekiya mfumu ya Yuda, atumiki ake ndi anthu onse, onse opulumuka ku mliri, lupanga ndi njala yaikulu mumzinda uwu, ndidzawapereka m’manja mwa Nebukadirezara mfumu ya Babulo. Ndidzawapereka m’manja mwa adani awo ndi m’manja mwa amene akufuna moyo wawo. Nebukadirezara adzawapha ndi lupanga+ ndipo sadzawamvera chisoni, kuwakomera mtima kapena kuwachitira chifundo.”’+
-