Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 51:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ine ndakuchimwirani kwambiri,+

      Ndipo ndachita chinthu choipa pamaso panu,+

      Choncho mukamalankhula mumalankhula zachilungamo,+

      Ndipo mukamaweruza, mumaweruza molungama.+

  • Yeremiya 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Uphunzirepo kanthu pa kuipa kwako+ ndipo zochita zako zosakhulupirika zikudzudzule.+ Dziwa izi, ndipo ona kuti kusiya kwako Yehova Mulungu wako ndi chinthu choipa ndi chowawa.+ Iwe sundiopa ine,’+ watero Yehova wa makamu, Ambuye Wamkulu Koposa.+

  • Ezekieli 36:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Choncho mudzakumbukira njira zanu zoipa ndi zochita zanu zimene sizinali zabwino.+ Mudzanyansidwa ndi zochita zanu, zolakwa zanu ndi zinthu zonyansa zimene munachita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena