-
Machitidwe 12:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Tsopano Herode atakonzeka kuti abweretse Petulo kwa anthu, usiku umenewo Petuloyo anali chigonere ali womangidwa ndi maunyolo awiri pakati pa asilikali awiri. Pakhomo panalinso alonda olondera ndende.
-