Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Asa anamukwiyira wamasomphenyayo. Kenako anamuika m’ndende n’kumumanga m’matangadza+ popeza anamupsera mtima kwambiri chifukwa cha nkhani imeneyi.+ Pa nthawi yomweyo, Asa anayamba kuponderezanso+ anthu ake ena.

  • Yeremiya 29:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 ‘Yehova wakuika kukhala wansembe m’malo mwa Yehoyada wansembe kuti ukhale woyang’anira wamkulu m’nyumba ya Yehova+ ndi kuti umange munthu aliyense wamisala+ amene akuchita zinthu ngati mneneri. Munthu woteroyo umuike m’matangadza, miyendo, manja ndi mutu womwe.+

  • Machitidwe 16:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Popeza kuti anamulamula zimenezi, iye anawaponya m’chipinda chamkati cha ndendeyo+ ndi kumanga mapazi awo m’matangadza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena