Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 25:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno khoma la mzindawo linabooledwa,+ ndipo amuna onse ankhondo anathawa usiku kudzera pachipata chimene chinali pakati pa makoma awiri, pafupi ndi munda wa mfumu.+ Akasidi+ anali atazungulira mzinda wonsewo, ndipo mfumuyo inayamba kuthawa+ kulowera cha ku Araba.+

  • Yeremiya 52:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno khoma la mzindawo linabooledwa,+ ndipo amuna onse ankhondo anayamba kuthawa.+ Iwo anatuluka mumzindawo usiku kudzera pachipata chimene chinali pakati pa makoma awiri, pafupi ndi munda wa mfumu,+ ndipo analowera njira yopita ku Araba. Apa n’kuti Akasidi atazungulira mzinda wonsewo.+

  • Ezekieli 33:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno m’chaka cha 12 kuchokera pamene tinatengedwa ukapolo, m’mwezi wa 10, pa tsiku lachisanu la mweziwo, kunafika munthu amene anapulumuka kuchokera ku Yerusalemu. Iye anandiuza+ kuti: “Mzinda uja wawonongedwa!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena