Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 18:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno Ahimazi+ mwana wa Zadoki anati: “Ndiloleni ndithamange ndikapereke uthenga kwa mfumu, chifukwa Yehova wamuweruza kuti amulanditse m’manja mwa adani ake.”+

  • Esitere 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Amtokomawo+ anathamanga ndi kupita mofulumira atakwera pamahatchi amene anali kuwagwiritsa ntchito potumikira mfumu. Anapita mofulumira+ chifukwa cha mawu a mfumu ndipo lamulo linachokera m’nyumba ya mfumu yokhala ndi mpanda wolimba kwambiri ya ku Susani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena