Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 26:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anaika malire ozungulira pamwamba pa madzi,+

      Kumene kuwala kumakathera mu mdima.

  • Yobu 38:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako ndinaiuza kuti, ‘Ukhoza kufika apa, koma usapitirirepo,+

      Ndipo mafunde ako aatali azilekezera pamenepa.’+

  • Salimo 33:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anasonkhanitsa madzi a m’nyanja ngati wachita kuwatchinga ndi khoma,+

      Anaika madzi amphamvu m’nyumba zosungiramo zinthu.

  • Salimo 104:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Munawaikira malire kuti asapitirire malirewo,+

      Kuti asamizenso dziko lapansi.+

  • Miyambo 8:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 pamene anaikira nyanja lamulo lake lakuti madzi ake asapitirire pamene anawalamula,+ pamene anakhazikitsa maziko a dziko lapansi,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena