Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 16:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Yehova ndiye gawo langa, gawo limene ndinapatsidwa,+ komanso chikho changa.+

      Inu mukundisungira bwino kwambiri cholowa changa.

  • Salimo 73:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Thupi langa ndi mtima wanga zalefuka.+

      Mulungu ndiye thanthwe la mtima wanga ndiponso cholowa changa mpaka kalekale.+

  • Salimo 119:57
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  57 Yehova, inu ndiye cholowa changa.+

      Ndalonjeza kusunga mawu anu.+

  • Salimo 142:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndinafuula kwa inu kuti mundithandize, inu Yehova.+

      Ndinanena kuti: “Inu ndinu pothawirapo panga,+

      Gawo langa+ m’dziko la amoyo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena