Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu oipa+ adzapita ku Manda,+

      Ngakhalenso anthu onse a mitundu ina amene aiwala Mulungu.+

  • Salimo 79:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tsanulirani mkwiyo wanu pa mitundu ya anthu amene akukunyalanyazani,+

      Ndi pa maufumu amene sakuitana pa dzina lanu.+

  • Yesaya 34:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pakuti Yehova wakwiyira mitundu yonse.+ Wapsera mtima asilikali awo onse.+ Iye awawononga ndipo awapha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena