Levitiko 26:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Chotero mudzadya ana anu aamuna ndi ana anu aakazi.+ Deuteronomo 28:55 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 55 kuti asagawireko aliyense wa iwo mnofu uliwonse wa ana ake aamuna amene adzawadya. Adzatero poona kuti alibiretu china chilichonse, chifukwa cha zovuta ndi nsautso zimene mdani wanu adzakupanikizani nazo m’mizinda yanu yonse.+ Maliro 2:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Inu Yehova, yang’anani kuti muone+ yemwe mwamulanga chotere.Kodi amayi azidya zipatso za mimba yawo, ana awo athanzi?+Kapena kodi wansembe ndi mneneri aziphedwa m’malo opatulika a Yehova?+ Maliro 4:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ngakhale mimbulu imapereka bere kwa ana ake kuti ayamwe.Koma mwana wamkazi wa anthu anga wakhala wankhanza+ ngati nthiwatiwa m’chipululu.+
55 kuti asagawireko aliyense wa iwo mnofu uliwonse wa ana ake aamuna amene adzawadya. Adzatero poona kuti alibiretu china chilichonse, chifukwa cha zovuta ndi nsautso zimene mdani wanu adzakupanikizani nazo m’mizinda yanu yonse.+
20 Inu Yehova, yang’anani kuti muone+ yemwe mwamulanga chotere.Kodi amayi azidya zipatso za mimba yawo, ana awo athanzi?+Kapena kodi wansembe ndi mneneri aziphedwa m’malo opatulika a Yehova?+
3 Ngakhale mimbulu imapereka bere kwa ana ake kuti ayamwe.Koma mwana wamkazi wa anthu anga wakhala wankhanza+ ngati nthiwatiwa m’chipululu.+