Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 102:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Koma inu simudzasintha, ndipo mudzakhalapo kwamuyaya.+

  • Salimo 145:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ufumu wanu ndi ufumu umene udzakhalapobe mpaka kalekale.+

      Ulamuliro wanu udzakhalapobe ku mibadwo yonse.+

  • Salimo 146:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yehova adzakhala mfumu mpaka kalekale,+

      Mulungu wako, iwe Ziyoni, adzakhala mfumu ku mibadwomibadwo.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Habakuku 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Yehova, inutu mwakhalapo kuyambira kalekale.+ Inu Mulungu wanga, Mulungu wanga Woyera, inu simufa.+ Inu Yehova, mwaika Akasidi pamalo oti muwaweruze. Inu Thanthwe,+ mwasankha kuti mutidzudzule.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena