Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 25:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Tsopano Aisiraeli anali kukhala ku Sitimu.+ Ali kumeneko, iwo anayamba kuchita chiwerewere ndi akazi a ku Mowabu.+

  • Deuteronomo 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova atakutumani kuchokera ku Kadesi-barinea+ kuti, ‘Kwerani ndi kukatenga dziko limene ndidzakupatsani kuti likhale lanu,’ pamenepo munapandukiranso malamulo a Yehova Mulungu wanu,+ ndipo simunasonyeze chikhulupiriro+ mwa iye komanso simunamvere mawu ake.+

  • 1 Mafumu 13:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno anayamba kuuza munthu wa Mulungu woona yemwe anachokera ku Yuda uja, kuti: “Nazi zimene Yehova wanena, ‘Chifukwa chakuti wapandukira+ lamulo la Yehova, ndipo sunasunge lamulo limene Yehova Mulungu wako anakulamula,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena