Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 20:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pambuyo pake mneneri Yesaya anapita kwa Mfumu Hezekiya n’kuifunsa kuti:+ “Kodi anthu aja anena kuti chiyani, ndipo anachokera kuti?”+ Hezekiya anayankha kuti: “Anachokera kudziko lakutali, ku Babulo.”

  • Yesaya 39:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pambuyo pake, mneneri Yesaya anapita kwa Mfumu Hezekiya n’kuifunsa kuti:+ “Kodi anthu aja anena kuti chiyani, ndipo anachokera kuti?” Hezekiya anayankha kuti: “Anachokera kudziko lakutali, ku Babulo.”+

  • Ezekieli 21:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Koma iwe mwana wa munthu, konza misewu iwiri yoti lupanga la mfumu ya Babulo lidzadutsemo.+ Misewu yonseyo ichokere m’dziko limodzi. Pamsewu wopita mumzindawo, uikepo chikwangwani cholozera kumeneko.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena