Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 24:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano Yehova anayamba kum’tumizira Yehoyakimu magulu a achifwamba a Akasidi,+ a Asiriya, a Amowabu,+ ndi a ana a Amoni. Ankawatumiza ku Yuda kuti awononge dzikolo mogwirizana ndi mawu a Yehova+ amene analankhula kudzera mwa atumiki ake, aneneri.

  • Yesaya 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Taonani dziko la Akasidi.+ Anthu awa, osati Asuri,+ ndi amene anapanga mzindawo kuti ukhale malo okhala nyama zam’chipululu.+ Amanga nsanja zawo zomenyerapo nkhondo.+ Agumula nyumba zake zachifumu.+ Iwo asandutsa mzindawo bwinja logumukagumuka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena