Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 20:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Anthuwo anafika ndi kumuzungulira ali mumzinda+ wa Abele wa ku Beti-maaka. Iwo anamanga chiunda chomenyerapo nkhondo* ndi mzindawo. Anthu onse amene anali ndi Yowabu anali kukumba pansi pa mpandawo kuti augwetse.

  • Ezekieli 21:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 M’dzanja lake lamanja, maulawo asonyeza kuti iye apite ku Yerusalemu, kuti akaike zida zogumulira mzindawo,+ akalamule asilikali ake kuti aphe anthu, akalize chizindikiro chochenjeza,+ akaike zida zogumulira zipata za mzindawo, ndiponso kuti akamange chiunda chomenyerapo nkhondo, ndi mpanda womenyerapo nkhondo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena