Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ansembe aja ataliza malipenga awo,+ asilikaliwo anafuula. Atangomva kulira kwa malipenga, anayamba kufuula mwamphamvu mfuu yankhondo, ndipo mpanda wa mzindawo unayamba kugwa mpaka pansi.+ Zitatero, iwo analowa mumzindawo. Aliyense anathamangira kumeneko, ndi kulanda mzindawo.

  • 1 Samueli 17:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Choncho Davide anadzuka m’mawa kwambiri, atasiya nkhosa zake m’manja mwa wozisamalira. Iye ananyamula katundu wake ndi kunyamuka monga mmene Jese, bambo ake, anamuuzira.+ Atafika mkati mwa mpanda wa msasa,+ anapeza asilikali akupita kumalo omenyera nkhondo,+ akufuula mfuwu ya nkhondo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena