Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndikanoladi lupanga langa lonyezimira,+

      Dzanja langa likagwira chiweruzo,+

      Ndidzalipsira adani anga,+

      Ndipo ndidzabwezera chilango kwa odana nane kwambiri.+

  • Salimo 17:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Nyamukani, inu Yehova, yang’anizanani naye maso ndi maso woipayo.+

      M’gonjetseni. Pulumutsani moyo wanga kwa woipayo ndi lupanga lanu.+

  • Ezekieli 32:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Lupanga la mfumu ya Babulo lidzafika pa iwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena