Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 19:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Munthu aliyense wokhudza mtembo, thupi la munthu aliyense amene angamwalire, amene sadzadziyeretsa, adzaipitsa chihema cha Yehova.+ Munthu ameneyo aphedwe kuti asakhalenso pakati pa Isiraeli.+ Iye ndi wodetsedwa chifukwa sanawazidwe madzi oyeretsera.+ Chidetso chake chikadali pa iye.+

  • Salimo 51:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndiyeretseni ndi hisope ku machimo anga kuti ndikhale woyera.+

      Ndisambitseni kuti ndiyere kwambiri kuposa chipale chofewa.+

  • Aheberi 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 tiyeni timufikire Mulungu ndi mitima yoona. Tichite zimenezi tilibe chikayikiro chilichonse komanso tili ndi chikhulupiriro, pakuti mitima yathu yayeretsedwa* kuti isakhalenso ndi chikumbumtima choipa,+ ndipo matupi athu asambitsidwa m’madzi oyera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena